Numeri 22:26 - Buku Lopatulika26 Pamenepo mthenga wa Yehova anapitiriranso, naima popapatiza, popanda popatukira kulamanja kapena kulamanzere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201426 Pamenepo mthenga wa Yehova anapitiriranso, naima popapatiza, popanda popatukira kulamanja kapena kulamanzere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa26 Kenaka mngelo wa Chauta adatsogolako nakaimiriranso pa malo ophaphatiza, opanda koti nkutembenukira kumanja kapena kumanzere. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero26 Kenaka mngelo wa Yehova anapita patsogolo ndi kuyima pamalo opanikizika pomwe panalibe poti nʼkutembenukira ku dzanja lamanja kapena lamanzere. Onani mutuwo |