Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 22:25 - Buku Lopatulika

25 Ndipo bulu anaona mthenga wa Yehova, nadzikankhira kulinga, nakanikiza phazi la Balamu kulinga; ndipo anampandanso.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Ndipo bulu anaona mthenga wa Yehova, nadzikankhira kulinga, nakanikiza phazi la Balamu kulinga; ndipo anampandanso.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Buluyo ataona mngelo wa Chauta, adadzipanikiza ku khoma, nakanikiza phazi la Balamu kukhomako. Pomwepo Balamu adamenya buluyo kachiŵiri.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Bulu uja ataona mngelo wa Yehova anadzipanikiza ku khoma, kukhukhuza phazi la Balaamu kukhomako. Ndipo pomwepo Balaamu anamenya buluyo kachiwiri.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 22:25
4 Mawu Ofanana  

Taima tsopano ndi maphendo ako, ndi unyinji wa matsenga ako, m'menemo iwe unagwira ntchito chiyambire ubwana wako; kuti kapena udzatha kupindula, kuti kapena udzapambana.


Pamenepo mthenga wa Yehova anaima m'njira yopapatiza ya minda yampesa; mbali ina kuli linga, mbali ina linga.


Pamenepo mthenga wa Yehova anapitiriranso, naima popapatiza, popanda popatukira kulamanja kapena kulamanzere.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa