Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 22:27 - Buku Lopatulika

27 Ndipo bulu wake anaona mthenga wa Yehova, nagona pansi, Balamu ali pamsana pake; ndipo Balamu adapsa mtima, nampanda bulu ndi ndodo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

27 Ndipo bulu wake anaona mthenga wa Yehova, nagona pansi, Balamu ali pamsana pake; ndipo Balamu adapsa mtima, nampanda bulu ndi ndodo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

27 Buluyo ataona mngelo wa Chauta, adagona pansi, Balamu ali pamsana pake. Balamu adapsa mtima kwambiri, namenya buluyo ndi ndodo yake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

27 Buluyo ataonanso mngelo wa Yehova uja, anagona pansi Balaamu ali pa msana, ndipo iye anakwiya ndi kumumenya ndi ndodo yake.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 22:27
4 Mawu Ofanana  

Wanzeru amaopa nasiya zoipa; koma wopusa amanyada osatekeseka.


Pamenepo mthenga wa Yehova anapitiriranso, naima popapatiza, popanda popatukira kulamanja kapena kulamanzere.


Mudziwa, abale anga okondedwa, kuti munthu aliyense akhale wotchera khutu, wodekha polankhula, wodekha pakupsa mtima.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa