Numeri 22:22 - Buku Lopatulika22 Koma anapsa mtima Mulungu chifukwa cha kupita iye, ndipo mthenga wa Yehova anadziika m'njira wotsutsana naye. Ndipo anali wokwera pabulu wake, ndi anyamata ake awiri anali naye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Koma anapsa mtima Mulungu chifukwa cha kupita iye, ndipo mthenga wa Yehova anadziika m'njira wotsutsana naye. Ndipo anali wokwera pa bulu wake, ndi anyamata ake awiri anali naye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Komabe Mulungu adapsa mtima chifukwa choti Balamuyo adapita. Ndipo mngelo wa Chauta adaimirira mu mseu, kuti amtsekere njira. Pamenepo nkuti atakwera bulu, ndipo ali ndi anyamata ake aŵiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Koma Mulungu anakwiya kwambiri pamene ankapita ndipo mngelo wa Yehova anayima pa njira kutsutsana naye. Balaamu anakwera bulu wake wamkazi ndipo antchito ake awiri anali naye. Onani mutuwo |