Numeri 22:15 - Buku Lopatulika15 Koma Balaki anaonjeza kutumanso akalonga, ochuluka, ndi omveka koposa awa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201415 Koma Balaki anaonjeza kutumanso akalonga, ochuluka, ndi omveka koposa awa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa15 Balaki adatumanso akalonga ochuluka ndi olemekezeka kopambana oyamba aja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero15 Kenaka Balaki anatumanso akuluakulu ena ambiri ndi olemekezeka kwambiri kuposa oyamba aja ndipo Onani mutuwo |