Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 22:14 - Buku Lopatulika

14 Pamenepo akalonga a Mowabu ananyamuka, nafika kwa Balaki, nati Alikukana Balamu kudza nafe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

14 Pamenepo akalonga a Mowabu ananyamuka, nafika kwa Balaki, nati Alikukana Balamu kudza nafe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

14 Tsono akalonga a Mowabu aja adanyamuka napita kwa Balaki, ndipo adakamuuza kuti, “Balamu wakana kubwera.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

14 Kotero akuluakulu a Mowabu anabwerera kwa Balaki ndi kukanena kuti, “Balaamu wakana kubwera nafe.”

Onani mutuwo Koperani




Numeri 22:14
3 Mawu Ofanana  

Ndipo Balamu anauka m'mawa, nati kwa akalonga a Balaki, Mukani ku dziko lanu; popeza Yehova andikaniza kuti ndisapite nanu.


Koma Balaki anaonjeza kutumanso akalonga, ochuluka, ndi omveka koposa awa.


Ndipo Balaki anati kwa Balamu, Kodi sindinatumize kwa iwe ndithu kukakuitana? Unalekeranji kudza kwa ine? Sindikhoza kodi kukuchitira ulemu?


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa