Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 22:10 - Buku Lopatulika

10 Ndipo Balamu anati kwa Mulungu, Balaki mwana wa Zipori mfumu ya Mowabu, anatumiza kwa ine, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 Ndipo Balamu anati kwa Mulungu, Balaki mwana wa Zipori mfumu ya Mowabu, anatumiza kwa ine, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 Balamu adayankha kuti, “Balaki mwana wa Zipora mfumu ya Mowabu, watumiza uthenga kudzandiwuza kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 Balaamu anayankha Mulungu kuti, “Balaki mwana wa Zipori, mfumu ya Mowabu, ananditumizira uthenga uwu:

Onani mutuwo Koperani




Numeri 22:10
3 Mawu Ofanana  

Taonani, anthu awa adatuluka mu Ejipito aphimba nkhope ya dziko, idzatu unditembererere awa; kapena ndidzakhoza kulimbana nao nkhondo, ndi kuwapirikitsa.


Ndipo Mulungu anadza kwa Balamu, nati, Anthu awa ali ndi iwe ndiwo ayani?


Ndipo anapha mafumu a Amidiyani pamodzi ndi ophedwa ao ena; ndiwo Evi, ndi Rekemu, ndi Zuri, ndi Huri, ndi Reba, mafumu asanu a Amidiyani; namupha Balamu mwana wa Beori ndi lupanga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa