Numeri 20:13 - Buku Lopatulika13 Awa ndi madzi a Meriba; popeza ana a Israele anatsutsana ndi Yehova, ndipo anapatulidwa mwa iwowa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Awa ndi madzi a Meriba; popeza ana a Israele anatsutsana ndi Yehova, ndipo anapatulidwa mwa iwowa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ameneŵa ndiwo madzi a ku Meriba kumene Aisraele adakangana ndi Chauta, ndipo Chauta adadziwonetsa pakati pa anthuwo kuti ndi woyera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Awa anali madzi a ku Meriba, kumene Aisraeli anakangana ndi Yehova ndiponso kumene Yehovayo anadzionetsa yekha kuti ndi Woyera pakati pawo. Onani mutuwo |