Numeri 20:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni, Popeza simunandikhulupirira Ine, kundipatula Ine pamaso pa ana a Israele, chifukwa chake simudzalowetsa msonkhano uwu m'dziko ndinawapatsali. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo Yehova ananena ndi Mose ndi Aroni, Popeza simunandikhulupirira Ine, kundipatula Ine pamaso pa ana a Israele, chifukwa chake simudzalowetsa msonkhano uwu m'dziko ndinawapatsali. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Chauta adauza Mose ndi Aroni kuti, “Popeza kuti simudandikhulupirire, ndipo simudasonyeze pamaso pa Aisraele kuti ndine woyera, simudzaŵaloŵetsa anthuŵa m'dziko limene ndaŵapatsa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Koma Yehova anati kwa Mose ndi Aaroni, “Chifukwa chakuti simunandikhulupirire ndiponso simunandilemekeze monga Woyera pamaso pa Aisraeli, simudzalowetsa anthuwa mʼdziko limene ndikupereka kwa iwo.” Onani mutuwo |