Numeri 20:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo Mose anasamula dzanja lake, napanda thanthwe kawiri ndi ndodo; ndipo madzi anatulukamo ochuluka, ndi khamulo linamwa, ndi zoweta zao zomwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo Mose anasamula dzanja lake, napanda thanthwe kawiri ndi ndodo; ndipo madzi anatulukamo ochuluka, ndi khamulo linamwa, ndi zoweta zao zomwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Apo Mose adakweza dzanja lake, namenya thanthwe kaŵiri ndi ndodo yake. Pompo mudatuluka madzi ambiri, ndipo mpingo wonsewo udamwa pamodzi ndi zoŵeta zomwe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Choncho Mose anatukula dzanja lake ndi kumenya thanthwelo kawiri ndi ndodo yake ndipo madzi ambiri anatuluka mwamphamvu, ndipo anthu ndi ziweto zawo anamwa. Onani mutuwo |