Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 2:21 - Buku Lopatulika

21 Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi atatu mphambu ziwiri kudza mazana awiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

21 Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi atatu mphambu ziwiri kudza mazana awiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

21 ndipo ankhondo ake ngokwanira 32,200.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

21 Chiwerengero cha gulu lake lankhondo ndi 32,200.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 2:21
4 Mawu Ofanana  

owerengedwa ao a fuko la Manase, ndiwo zikwi makumi atatu mphambu ziwiri kudza mazana awiri.


Ndipo oyandikizana naye ndiwo a fuko la Manase; ndi kalonga wa ana a Manase ndiye Gamaliele mwana wa Pedazuri.


Ndi fuko la Benjamini: kalonga wa ana a Benjamini ndiye Abidani mwana wa Gideoni.


Iwo ndiwo mabanja ao a Manase; ndipo owerengedwa ao ndiwo zikwi makumi asanu mphambu ziwiri kudza mazana asanu ndi awiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa