Numeri 19:7 - Buku Lopatulika7 Pamenepo wansembe atsuke zovala zake, nasambe thupi lake ndi madzi; ndipo atatero alowenso kuchigono; koma wansembeyo adzakhala wodetsedwa kufikira madzulo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Pamenepo wansembe atsuke zovala zake, nasambe thupi lake ndi madzi; ndipo atatero alowenso kuchigono; koma wansembeyo adzakhala wodetsedwa kufikira madzulo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Tsono wansembe achape zovala zake, ndipo asambe thupi lonse, pambuyo pake aloŵe m'mahema. Koma wansembeyo adzakhale woipitsidwa mpaka madzulo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Zitatha izi, wansembeyo ayenera kuchapa zovala zake ndiponso asambe ndi madzi. Iye angathe kupita ku msasa, komabe adzakhala wodetsedwa mpaka madzulo. Onani mutuwo |
Ndipo chilichonse chakufa cha izi chikagwera kanthu, kanthuka kadzakhala kodetsedwa; ngakhale chipangizo chamtengo, kapena chovala, kapena chikopa kapena thumba, chipangizo chilichonse chimene agwira nacho ntchito, achiviike m'madzi, ndipo chidzakhala chodetsedwa kufikira madzulo; pamenepo chidzakhala choyera.