Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 16:44 - Buku Lopatulika

44 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

44 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

44 ndipo Chauta adauza Moseyo kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

44 ndipo Yehova anawuza Mose kuti,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 16:44
4 Mawu Ofanana  

Arauna nati, Mbuye wanga mfumu, mwadzeranji kwa mnyamata wanu? Ndipo Davide, anati, Kugula dwale lako ili, kuti ndimangirepo Yehova guwa la nsembe, kuti mliriwo ulekeke kwa anthu.


Koma Iye pokhala ngwa chifundo, anakhululukira choipa, osawaononga; nabweza mkwiyo wake kawirikawiri, sanautse ukali wake wonse.


Ndipo Mose ndi Aroni anadza kukhomo kwa chihema chokomanako.


Kwerani kuchoka pakati pa khamu lino, kuti ndiwathe m'kamphindi. Pamenepo adagwa nkhope zao pansi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa