Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 16:25 - Buku Lopatulika

25 Ndipo Mose anauka namuka kwa Datani ndi Abiramu; ndi akulu a Israele anamtsata.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 Ndipo Mose anauka namuka kwa Datani ndi Abiramu; ndi akulu a Israele anamtsata.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Tsono Mose adapita kwa Datani ndi Abiramu, ndipo akuluakulu a Aisraele adamtsatira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Mose anayimirira napita kwa Datani, Abiramu ndi kwa akuluakulu a Israeli amene ankamutsatira.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 16:25
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anatsika mumtambo, nanena naye, natengako mzimu uli pa iye, nauika pa akulu makumi asanu ndi awiri; ndipo kunali kuti pokhala mzimu pa iwowa, ananenera; koma osabwerezanso.


Ndipo Mose ndi akulu onse a Israele anasonkhana kuchigono.


Koma Kora, mwana wa Izihara, mwana wa Kohati, mwana wa Levi, anatenga Datani ndi Abiramu, ana a Eliyabu, ndi Oni mwana wa Peleti, ana a Rubeni;


Nena ndi khamulo, ndi kuti, Kwerani kuchoka pozungulira mahema a Kora, Datani, ndi Abiramu.


Ndipo ananena ndi khamulo, nati, Chokanitu ku mahema a anthu awa oipa, musamakhudza kanthu kao kalikonse, mungaonongeke m'zochimwa zao zonse.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa