Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 16:24 - Buku Lopatulika

24 Nena ndi khamulo, ndi kuti, Kwerani kuchoka pozungulira mahema a Kora, Datani, ndi Abiramu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

24 Nena ndi khamulo, ndi kuti, Kwerani kuchoka pozungulira mahema a Kora, Datani, ndi Abiramu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

24 “Uza mpingo kuti achoke pafupi ndi mahema a Kora, Datani ndi Abiramu.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

24 “Uza gulu lonse kuti, ‘Khalani kutali ndi matenti a Kora, Datani ndi Abiramu.’ ”

Onani mutuwo Koperani




Numeri 16:24
5 Mawu Ofanana  

Koma Kora, mwana wa Izihara, mwana wa Kohati, mwana wa Levi, anatenga Datani ndi Abiramu, ana a Eliyabu, ndi Oni mwana wa Peleti, ana a Rubeni;


Dzipatuleni pakati pa khamu lino, kuti ndiwathe m'kamphindi.


Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,


Ndipo Mose anauka namuka kwa Datani ndi Abiramu; ndi akulu a Israele anamtsata.


Kwerani kuchoka pakati pa khamu lino, kuti ndiwathe m'kamphindi. Pamenepo adagwa nkhope zao pansi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa