Numeri 15:40 - Buku Lopatulika40 kuti mukumbukire ndi kuchita malamulo anga onse, ndi kukhala wopatulikira Mulungu wanu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201440 kuti mukumbukire ndi kuchita malamulo anga onse, ndi kukhala wopatulikira Mulungu wanu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa40 Choncho mudzakumbukira ndi kugwiritsa ntchito malamulo anga onse, mudzakhala oyera mtima pamaso pa Mulungu wanu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero40 Motero mudzakumbukira kumvera malamulo anga ndipo mudzakhala opatulikira a Mulungu wanu. Onani mutuwo |