Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 15:17 - Buku Lopatulika

17 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Ndipo Yehova ananena ndi Mose, nati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 Chauta adauza Mose kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Yehova anawuza Mose kuti,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 15:17
4 Mawu Ofanana  

Mutuluke nayo m'zinyumba zanu mikate iwiri ya nsembe yoweyula, ikhale ya awiri a magawo khumi a efa; ikhale ya ufa wosalala, yopanga ndi chotupitsa, zipatso zoyamba za Yehova.


Pakhale chilamulo chimodzi ndi chiweruzo chimodzi kwa inu ndi kwa mlendo wakukhala kwanu.


Nena ndi ana a Israele, nuti nao, Pamene mulowa m'dziko limene ndilikukulowetsani,


Ndipo ngati zipatso zoyamba zili zopatulika, choteronso mtanda; ndipo ngati muzu uli wopatulika, choteronso nthambi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa