Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 15:12 - Buku Lopatulika

12 Monga mwa kuwerenga kwake kwa izi muzikonza, muzitero ndi yonse monga mwa kuwerenga kwake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Monga mwa kuwerenga kwake kwa izi muzikonza, muzitero ndi yonse monga mwa kuwerenga kwake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Zingachuluke chotani nyama zoperekedwazo, muchite choncho ndi nyama iliyonse, mpaka zonse kutha.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Ngakhale zingachuluke chotani, chitani izi kwa iliyonse ya nyamazo.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 15:12
2 Mawu Ofanana  

Kudzatero ndi ng'ombe iliyonse, kapena nkhosa yamphongo iliyonse, kapena mwanawankhosa aliyense, kapena mwanawambuzi aliyense.


Onse akubadwa m'dzikomo achite izi momwemo, pobwera nayo kwa Yehova nsembe yamoto ya fungo lokoma.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa