Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 15:13 - Buku Lopatulika

13 Onse akubadwa m'dzikomo achite izi momwemo, pobwera nayo kwa Yehova nsembe yamoto ya fungo lokoma.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Onse akubadwa m'dzikomo achite izi momwemo, pobwera nayo kwa Yehova nsembe yamoto ya fungo lokoma.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Mbadwa zonse zizichita motero pamene zikupereka nsembe yotentha pa moto, yotulutsa fungo lokomera Chauta.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 “ ‘Mbadwa iliyonse ya mu Israeli izichita zimenezi pamene ibweretsa nsembe yotentha pa moto kuti ikhale fungo lokoma kwa Yehova.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 15:13
2 Mawu Ofanana  

Monga mwa kuwerenga kwake kwa izi muzikonza, muzitero ndi yonse monga mwa kuwerenga kwake.


Ndipo akakhala nanu mlendo, kapena aliyense wakukhala pakati pa inu mwa mibadwo yanu, nakachitira Yehova nsembe yamoto ya fungo lokoma; monga muchita inu, momwemo iyenso,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa