Numeri 14:7 - Buku Lopatulika7 nanena ndi khamu lonse la ana a Israele, nati, Dziko tapitamo kulizonda, ndilo dziko lokometsetsa ndithu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 nanena ndi khamu lonse la ana a Israele, nati, Dziko tapitamo kulizonda, ndilo dziko lokometsetsa ndithu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Ndipo adauza mpingo wonse wa Aisraele uja kuti, “Dziko limene tidakalizondalo ndi labwino kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 ndipo anati kwa gulu lonse la Aisraeli, “Dziko limene tinakayendamo ndi kuliona ndi labwino kwambiri zedi. Onani mutuwo |