Numeri 14:5 - Buku Lopatulika5 Pamenepo Mose ndi Aroni anagwa nkhope pansi pamaso pa msonkhano wonse wa khamu la ana a Israele. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Pamenepo Mose ndi Aroni anagwa nkhope pansi pamaso pa msonkhano wonse wa khamu la ana a Israele. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Mose ndi Aroni adadziponya pansi pamaso pa mpingo wonse wa Aisraele. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Koma Mose ndi Aaroni anadzigwetsa pansi chafufumimba pamaso pa Aisraeli onse omwe anasonkhana pamenepo. Onani mutuwo |