Numeri 14:44 - Buku Lopatulika44 Koma anakwera pamwamba paphiri modzikuza; koma likasa la chipangano la Yehova, ndi Mose, sanachoke kuchigono. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201444 Koma anakwera pamwamba pa phiri modzikuza; koma likasa la chipangano la Yehova, ndi Mose, sanachoke kuchigono. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa44 Koma iwo adapitabe osasamala, nakwera ku dziko lamapiri, ngakhale kuti sadatsakane ndi Bokosi lachipangano cha Chauta, kapena ndi Mose, pochoka pamahemapo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero44 Komabe mwa maganizo awo anapita molunjika dziko la mapiri ngakhale kuti Mose sanachoke ndi Bokosi la Chipangano la Yehova pa msasa. Onani mutuwo |