Numeri 14:45 - Buku Lopatulika45 Pamenepo anatsika Aamaleke, ndi Akanani, akukhala m'phirimo nawakantha, nawapha kufikira ku Horoma. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201445 Pamenepo anatsika Aamaleke, ndi Akanani, akukhala m'phirimo nawakantha, nawapha kufikira ku Horoma. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa45 Tsono Aamaleke ndi Akanani, amene ankakhala m'dziko lamapirilo, adatsika ndipo adaŵagonjetsa, ndi kuŵapirikitsa mpaka ku Horoma. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero45 Koma Aamaleki ndi Akanaani amene ankakhala ku dziko lamapirilo anatsika ndi kumenyana nawo ndipo anawakantha mʼnjira yonse mpaka ku Horima. Onani mutuwo |