Numeri 14:28 - Buku Lopatulika28 Nunene nao, Pali Ine ati Yehova, ndidzachitira inu ndithu monga mwanena m'makutu mwanga; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201428 Nunene nao, Pali Ine ati Yehova, ndidzachitira inu ndithu monga mwanena m'makutu mwanga; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa28 Uŵauze kuti, Chauta akunena kuti, ‘Zimene mwanena, Ine ndamva, ndipo ndi zimene ndidzakuchitani. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero28 Tsono awuze kuti, ‘Ndikulumbira pali Ine,’ akutero Yehova, ‘Ndidzakuchitirani zinthu zonse zimene ndamva inu mukunena: Onani mutuwo |