Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 14:26 - Buku Lopatulika

26 Ndipo Yehova ananena kwa Mose ndi Aroni, nati,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

26 Ndipo Yehova ananena kwa Mose ndi Aroni, nati,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

26 Chauta adafunsa Mose ndi Aroni kuti,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

26 Yehova anawuza Mose ndi Aaroni kuti,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 14:26
3 Mawu Ofanana  

Koma Aamaleke ndi Akanani akhala m'chigwamo; tembenukani mawa, nimunke ulendo wanu kuchipululu, njira ya ku Nyanja Yofiira.


Ndileke khamu loipa ili lakudandaula pa Ine kufikira liti? Ndidamva madandaulo a ana a Israele, amene amandidandaulira.


Popeza Yehova adanena za iwowa, Adzafatu m'chipululu. Ndipo sanatsalire mmodzi wa iwowa koma Kalebe mwana wa Yefune, ndi Yoswa mwana wa Nuni.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa