Numeri 14:16 - Buku Lopatulika16 Popeza Yehova sanakhoze kuwalowetsa anthu awa m'dziko limene anawalumbirira, chifukwa chake anawapha m'chipululu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Popeza Yehova sanakhoze kuwalowetsa anthu awa m'dziko limene anawalumbirira, chifukwa chake anawapha m'chipululu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 ‘Chauta waŵaphera m'chipululu anthuŵa, chifukwa choti sadathe kuŵaloŵetsa m'dziko limene adalumbira kuti adzaŵapatsa kuti likhale lao.’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 ‘Yehova walephera kuwalowetsa anthuwo mʼdziko lomwe anawalonjeza molumbira, ndipo wawapha mʼchipululu.’ Onani mutuwo |