Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 14:15 - Buku Lopatulika

15 Ndipo mukapha anthu awa ngati munthu mmodzi, pamenepo amitundu amene adamva mbiri yanu adzanena, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

15 Ndipo mukapha anthu awa ngati munthu mmodzi, pamenepo amitundu amene adamva mbiri yanu adzanena, ndi kuti,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

15 Tsopano mukaŵapha onse anthu ameneŵa, mitundu ina imene yamva mbiri yanu idzati,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

15 Tsono mukawapha anthu onsewa nthawi imodzi, mayiko amene anamva za Inu adzati,

Onani mutuwo Koperani




Numeri 14:15
3 Mawu Ofanana  

Akaneneranji Aejipito, ndi kuti, Anawatulutsa ndi cholinga choipa, kuti awaphe m'mapiri, ndi kuwatha pankhope padziko lapansi? Pepani, lekani choipacho cha pa anthu anu.


Popeza Yehova sanakhoze kuwalowetsa anthu awa m'dziko limene anawalumbirira, chifukwa chake anawapha m'chipululu.


Ndipo Yehova ananena naye, Popeza Ine ndidzakhala nawe udzakantha Amidiyani ngati munthu mmodzi.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa