Numeri 14:17 - Buku Lopatulika17 Ndipo tsopano, ikuletu mphamvu ya Mbuye wanga, monga mudanena, ndi kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Ndipo tsopano, ikuletu mphamvu ya Mbuye wanga, monga mudanena, ndi kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Tsono ndikukupemphani, Chauta muwonetse kuti mphamvu zanu nzazikulu monga mudalonjezera kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 “Chonde Ambuye wonetsani mphamvu yanu monga munalonjezera kuti, Onani mutuwo |