Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 13:30 - Buku Lopatulika

30 Koma Kalebe anatontholetsa anthu pamaso pa Mose, nati, Tikwere ndithu ndi kulilandira lathulathu; popeza tikhozadi kuchita kumene.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

30 Koma Kalebe anatontholetsa anthu pamaso pa Mose, nati, Tikwere ndithu ndi kulilandira lathulathu; popeza tikhozadi kuchita kumene.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

30 Koma Kalebe adaŵakhalitsa chete anthu pamaso pa Mose, nati, “Tiyeni tipite nthaŵi yomwe ino, tikalande dzikolo, chifukwa tingathe kuligonjetsa.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

30 Koma Kalebe anawakhalitsa chete anthuwo pamaso pa Mose, ndipo anati, “Tiyeni tipite ndithu ndi kutenga dzikolo, pakuti tingathe kulitenga.”

Onani mutuwo Koperani




Numeri 13:30
14 Mawu Ofanana  

Mwa Mulungu tidzachita molimbika mtima, ndipo Iye adzapondereza otisautsa.


Aamaleke akhala m'dziko la kumwera; ndi Ahiti, ndi Ayebusi, ndi Aamori, akhala ku mapiri, ndi Akanani akhala kunyanja, ndi m'mphepete mwa Yordani.


Koma anthu adakwera nayewo anati, Sitingathe kuwakwerera anthuwo; popeza atiposa mphamvu.


koma mtumiki wanga Kalebe, popeza anali nao mzimu wina, nanditsata monsemo, ndidzamlowetsa iyeyu m'dziko muja analowamo; ndi mbeu zake zidzakhala nalo.


Maina a amunawo ndiwo: wa fuko la Yuda, Kalebe mwana wa Yefune.


Ndipo tidzatani ndi zinthu izi? Ngati Mulungu ali ndi ife, adzatikaniza ndani?


Koma m'zonsezi, ife tilakatu, mwa Iye amene anatikonda.


Ndikhoza zonse mwa Iye wondipatsa mphamvuyo.


amene mwa chikhulupiriro anagonjetsa maufumu, anachita chilungamo, analandira malonjezano, anatseka pakamwa pa mikango,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa