Numeri 13:17 - Buku Lopatulika17 Potero Mose anawatuma azonde dziko la Kanani, nanena nao, Kwerani uko kumwera, nimukwere kumapiri; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Potero Mose anawatuma azonde dziko la Kanani, nanena nao, Kwerani uko kumwera, nimukwere kumapiri; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Mose adaŵatuma kukazonda dziko la Kanani, naŵauza kuti, “Pitani cha ku Negebu, ndipo mukakwere dziko lamapirilo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Mose atawatuma kuti akazonde Kanaani anati, “Mupite kudzera ku Negevi, mukapitirire mpaka ku dziko la mapiri. Onani mutuwo |