Numeri 13:16 - Buku Lopatulika16 Awa ndi maina a amunawo Mose anawatumira azonde dziko. Ndipo Mose anamutcha Hoseya mwana wa Nuni Yoswa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Awa ndi maina a amunawo Mose anawatumira azonde dziko. Ndipo Mose anamutcha Hoseya mwana wa Nuni Yoswa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Ameneŵa ndiwo maina a anthu amene Mose adaŵatuma kukazonda dziko. Ndipo Hoseya mwana wa Nuni, Mose adamutcha dzina loti Yoswa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Amenewa ndiwo mayina a anthu amene Mose anawatuma kukazonda dzikolo. (Hoseya mwana wa Nuni, Mose anamupatsa dzina loti Yoswa). Onani mutuwo |