Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 11:9 - Buku Lopatulika

9 Ndipo pakugwa mame pachigono usiku, mana anagwapo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndipo pakugwa mame pachigono usiku, mana anagwapo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Pamene mame ankagwa usiku pamahemapo, ankagwera kumodzi ndi mana.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Mame akamagwa pa msasawo usiku ankagwera kumodzi ndi manawo.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 11:9
6 Mawu Ofanana  

Anafunsa ndipo Iye anadzetsa zinziri, nawakhutitsa mkate wakumwamba.


Ndipo Mose anamva anthu alikulira m'mabanja ao, yense pakhomo pa hema wake; ndipo Yehova anapsa mtima ndithu, ndipo kudamuipira Mose.


Anthu amanka, nawaola, nawapera ndi mphero, kapena kuwasinja mumtondo, nawaphika m'mphika, nawaumba timitanda; ndi powalawa anali ngati timitanda tokazinga ndi mafuta.


Chiphunzitso changa chikhale ngati mvula; maneno anga agwe ngati mame; ngati mvula yowaza pamsipu, ndi monga madontho a mvula pazitsamba.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa