Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Numeri 11:9 - Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

9 Mame akamagwa pa msasawo usiku ankagwera kumodzi ndi manawo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Lopatulika

9 Ndipo pakugwa mame pachigono usiku, mana anagwapo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

9 Ndipo pakugwa mame pachigono usiku, mana anagwapo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

9 Pamene mame ankagwa usiku pamahemapo, ankagwera kumodzi ndi mana.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 11:9
6 Mawu Ofanana  

Iwo anapempha, ndipo Iye anawabweretsera zinziri ndipo anawakhutitsa ndi chakudya chochokera kumwamba.


Mose anamva anthu a banja lililonse akufuwula, banja lililonse pa khomo la tenti yake. Yehova anakwiya kwambiri ndipo Mose anavutikanso mu mtima.


Anthu ankapita kukatola manawo, nʼkumasinja mu mtondo kapena kupera. Ankawaphika mu mʼphika kapena kupanga makeke. Ndipo ankakoma ngati makeke ophikira mafuta a olivi.


Chiphunzitso changa chigwe ngati mvula ndipo mawu anga atsike ngati mame, ngati mvumbi pa udzu watsopano, ngati mvula yochuluka pa zomera zanthete.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa