Numeri 10:30 - Buku Lopatulika30 Koma anati kwa iye, Sindidzamuka nanu; koma ndipita ku dziko langa, ndi kwa abale anga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Koma anati kwa iye, Sindidzamuka nanu; koma ndipita ku dziko langa, ndi kwa abale anga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Koma iye adayankha kuti, “Sindipita nao, ndipita kwathu kwa abale anga.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Hobabu anayankha kuti, “Ayi, sindipita nanu, ndibwerera ku dziko la kwathu ndi kwa abale anga.” Onani mutuwo |