Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 10:13 - Buku Lopatulika

13 Potero anayamba ulendo wao monga mwa mau a Yehova ndi dzanja la Mose.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

13 Potero anayamba ulendo wao monga mwa mau a Yehova ndi dzanja la Mose.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

13 Kameneka kanali koyamba kuti Aisraele anyamuke, Chauta atalamula kudzera mwa Mose.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

13 Kameneka kanali koyamba kuti Aisraeli anyamuke monga momwe Yehova analamulira Mose.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 10:13
4 Mawu Ofanana  

Ndipo anayamba kuyenda ambendera ya chigono cha ana a Yuda monga mwa magulu ao; woyang'anira gulu lake ndiye Nasoni mwana wa Aminadabu.


Ndipo pokhala mtambo pamwamba pa chihema masiku pang'ono; pamenepo anakhala m'chigono monga awauza Yehova, nayendanso ulendo monga anauza Yehova.


Powauza Yehova amanga mahema, powauza Yehova ayenda ulendo; anasunga udikiro wa Yehova powauza Yehova mwa dzanja la Mose.


Yehova Mulungu wathu ananena ndi ife mu Horebu, ndi kuti Yakwanira nthawi yokhala inu m'phiri muno;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa