Numeri 10:13 - Buku Lopatulika13 Potero anayamba ulendo wao monga mwa mau a Yehova ndi dzanja la Mose. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Potero anayamba ulendo wao monga mwa mau a Yehova ndi dzanja la Mose. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Kameneka kanali koyamba kuti Aisraele anyamuke, Chauta atalamula kudzera mwa Mose. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Kameneka kanali koyamba kuti Aisraeli anyamuke monga momwe Yehova analamulira Mose. Onani mutuwo |