Numeri 1:50 - Buku Lopatulika50 koma iwe, uike Alevi asunge chihema cha mboni, ndi zipangizo zake zonse, ndi zonse ali nazo; azinyamula chihema, ndi zipangizo zake zonse; namtumikire, namange mahema ao pozungulira pa chihema. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201450 koma iwe, uike Alevi asunge Kachisi wa mboni, ndi zipangizo zake zonse, ndi zonse ali nazo; azinyamula Kachisi, ndi zipangizo zake zonse; namtumikire, namange mahema ao pozungulira pa Kachisi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa50 Uike Aleviwo kuti aziyang'anira chihema changa chaumboni, zipangizo zake ndi zonse zimene zili m'menemo. Azinyamula chihemacho, pamodzi ndi zipangizo zake, ndipo azichisamala. Zithando zao azimange pozungulira chihemacho. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero50 Koma uyike Aleviwo kuti aziyangʼanira tenti yanga yopatulika, zipangizo zake ndi zonse zili mʼmenemo. Azinyamula tentiyo pamodzi ndi zipangizo zake zonse; azisamalira ndi kumanga misasa mozungulira tentiyo. Onani mutuwo |