Numeri 1:49 - Buku Lopatulika49 Fuko la Levi lokha usaliwerenge, kapena kuona kufikira kwao mwa ana a Israele; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201449 Fuko la Levi lokha usaliwerenge, kapena kuona kufikira kwao mwa ana a Israele; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa49 “Fuko la Levi usaliŵerenge ai, anthu ake usaŵalembere kumodzi ndi Aisraele enawo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero49 “Usawerenge fuko la Levi kapena kuliphatikiza mʼkawundula wa Aisraeli. Onani mutuwo |