Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 1:43 - Buku Lopatulika

43 owerengedwa ao a fuko la Nafutali, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zitatu kudza mazana anai.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

43 owerengedwa ao a fuko la Nafutali, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zitatu kudza mazana anai.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

43 Tsono ataŵerenga maina onse a m'fuko la Nafutali, adapezeka kuti ali 53,400.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

43 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Nafutali chinali 53,400.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 1:43
4 Mawu Ofanana  

A ana a Nafutali, kubadwa kwao, monga mwa mabanja ao, monga mwa nyumba za makolo ao, powerenga maina, kuyambira a zaka makumi awiri ndi mphambu, onse akutulukira kunkhondo;


Iwo ndiwo amene anawerengedwa, amene Mose anawerenga pamodzi ndi Aroni, ndi akalonga a Israele, ndiwo amuna khumi ndi awiri; yense kunenera nyumba ya kholo lake.


Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zitatu kudza mazana anai.


Iwo ndiwo mabanja a Nafutali, monga mwa mabanja ao; ndipo owerengedwa ao ndiwo zikwi makumi anai mphambu zisanu kudza mazana anai.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa