Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 1:23 - Buku Lopatulika

23 owerengedwa ao a fuko la Simeoni, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zisanu ndi zinai kudza mazana atatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 owerengedwa ao a fuko la Simeoni, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zisanu ndi zinai kudza mazana atatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Tsono ataŵerenga maina onse a m'fuko la Simeoni, adapezeka kuti ali 59,300.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Simeoni chinali 59,300.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 1:23
6 Mawu Ofanana  

A ana a Simeoni, kubadwa kwao, monga mwa mabanja ao, monga mwa nyumba za makolo ao, owerengedwa ao, powerenga maina mmodzimmodzi, amuna onse kuyambira a zaka makumi awiri ndi mphambu, onse akutulukira kunkhondo;


A ana a Gadi, kubadwa kwao, monga mwa mabanja ao, powerenga maina, kuyambira a zaka makumi awiri ndi mphambu, onse akutulukira kunkhondo;


Ndi khamu lake ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zisanu ndi zinai kudza mazana atatu.


Koma dzina la Mwisraele adamuphayo, ndiye amene adamupha pamodzi ndi mkazi Mmidiyani, ndiye Zimiri mwana wa Salu, mfumu ya nyumba ya makolo mwa Asimeoni.


Iwo ndiwo mabanja a Asimeoni, zikwi makumi awiri mphambu ziwiri kudza mazana ziwiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa