Numeri 1:23 - Buku Lopatulika23 owerengedwa ao a fuko la Simeoni, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zisanu ndi zinai kudza mazana atatu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 owerengedwa ao a fuko la Simeoni, ndiwo zikwi makumi asanu mphambu zisanu ndi zinai kudza mazana atatu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Tsono ataŵerenga maina onse a m'fuko la Simeoni, adapezeka kuti ali 59,300. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Simeoni chinali 59,300. Onani mutuwo |