Nehemiya 9:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo munapenya msauko wa makolo athu mu Ejipito, nimunamva kufuula kwao ku Nyanja Yofiira, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo munapenya msauko wa makolo athu m'Ejipito, nimunamva kufuula kwao ku Nyanja Yofiira, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 “Mudaona kuzunzika kwa makolo athu ku Ejipito kuja, ndipo mudamva kulira kwao ku Nyanja Yofiira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 “Munaona kuzunzika kwa makolo athu ku Igupto. Munamva kufuwula kwawo pa Nyanja Yofiira. Onani mutuwo |