Nehemiya 9:8 - Buku Lopatulika8 ndipo munampeza mtima wake wokhulupirika pamaso panu, nimunapangana naye kumpatsa dziko la Akanani, Ahiti, Aamori, ndi Aperizi, ndi Ayebusi, ndi Agirigasi, kulipereka kwa mbumba zake; ndipo mwakwaniritsa mau anu, popeza Inu ndinu wolungama. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 ndipo munampeza mtima wake wokhulupirika pamaso panu, nimunapangana naye kumpatsa dziko la Akanani, Ahiti, Aamori, ndi Aperizi, ndi Ayebusi, ndi Agirigasi, kulipereka kwa mbumba zake; ndipo mwakwaniritsa mau anu, popeza Inu ndinu wolungama. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Mudaona kuti mtima wake unali wokhulupirika kwa Inu, ndipo mudachita naye chipangano chakuti zidzukulu zake mudzazipatsa dziko la Akanani, la Ahiti, la Aamori, la Aperezi, la Ayebusi ndi la Agirigasi. Mudachitadi zimene mudalonjezazo, pakuti Inu ndinu olungama. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Inu munaona kuti mtima wake unali wokhulupirika kwa inu, ndipo munapangana naye pangano lakuti mudzapereka kwa zidzukulu zake dziko la Akanaani Ahiti, Aamori, Aperezi, Ayebusi ndi Agirigasi. Inu mwasunga lonjezo lanu chifukwa ndinu wolungama. Onani mutuwo |