Nehemiya 9:7 - Buku Lopatulika7 Inu ndinu Yehova Mulungu amene munasankha Abramu ndi kumtulutsa mu Uri wa kwa Akaldeya, ndi kumutcha dzina lake Abrahamu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Inu ndinu Yehova Mulungu amene munasankha Abramu ndi kumtulutsa m'Uri wa Ababiloni, ndi kumutcha dzina lake Abrahamu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Inu ndinu Chauta, Mulungu amene mudasankha Abramu, kumtulutsa ku Uri wa ku Kaldeya, ndi kumutcha dzina loti Abrahamu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 “Inu ndinu Yehova Mulungu amene munasankha Abramu ndi kumutulutsa mʼdziko la Uri wa ku Kaldeya ndi kumutcha dzina lake Abrahamu. Onani mutuwo |