Nehemiya 9:32 - Buku Lopatulika32 Ndipo tsono, Mulungu wathu, ndinu Mulungu wamkulu, ndi wamphamvu, ndi woopsa, wakusunga pangano ndi chifundo, asachepe pamaso panu mavuto athu onse amene anatigwera ife, ndi mafumu athu, akulu athu, ndi ansembe athu, ndi aneneri athu, ndi makolo athu, ndi anthu anu onse, kuyambira masiku a mafumu a Asiriya, mpaka lero lino. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Ndipo tsono, Mulungu wathu, ndinu Mulungu wamkulu, ndi wamphamvu, ndi woopsa, wakusunga pangano ndi chifundo, asachepe pamaso panu mavuto athu onse amene anatigwera ife, ndi mafumu athu, akulu athu, ndi ansembe athu, ndi aneneri athu, ndi makolo athu, ndi anthu anu onse, kuyambira masiku a mafumu a Asiriya, mpaka lero lino. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 “Nchifukwa chake tsono, Inu Mulungu wathu, Mulungu wamkulu, wamphamvu ndi woopsa, mumasunga chipangano ndi chikondi chanu chosasinthika. Musalole kuti zosautsa zathu zonse zikuwonekereni ngati zochepa. Zosautsazo zatigwera ife, mafumu athu, akulu athu, ansembe athu, aneneri athu, makolo athu, ndiponso anthu anu onse, kuyambira nthaŵi ya mafumu a ku Asiriya mpaka lero lino. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 “Nʼchifukwa chake, tsono, Inu Mulungu wathu, Mulungu wamkulu, wamphamvu ndi woopsa kwambiri mumasunga pangano ndi chikondi chosasinthika. Musalole kuti mavuto onse amene atigwera ife, mafumu athu, atsogoleri athu, ansembe athu, aneneri athu, makolo athu ndi anthu ena onse kuyambira nthawi ya mafumu a ku Asiriya mpaka lero aoneke ochepa pamaso panu. Onani mutuwo |