Nehemiya 9:33 - Buku Lopatulika33 Koma Inu ndinu wolungama mwa zonse zatigwera; pakuti mwachita zoona, koma ife tachita choipa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201433 Koma Inu ndinu wolungama mwa zonse zatigwera; pakuti mwachita zoona, koma ife tachita choipa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa33 Komabe Inu mwakhala olungama pa zonse zimene zatigwera, ndipo mwachita zokhulupirika, koma ife tachita zolakwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero33 Koma Inu mwakhala wolungama pa zonse zimene zakhala zikutichitikira. Mwachita zokhulupirika, koma ife tachita zolakwa. Onani mutuwo |