Nehemiya 9:31 - Buku Lopatulika31 Ndipo mwa nsoni zanu zochuluka simunawathe, kapena kuwataya; popeza Inu ndinu Mulungu wa chisomo ndi chifundo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201431 Ndipo mwa nsoni zanu zochuluka simunawatha, kapena kuwataya; popeza Inu ndinu Mulungu wa chisomo ndi chifundo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa31 Ngakhale zinali choncho, Inu simudaŵaononge kotheratu, kapena kuŵasiya, pakuti Inu ndinu Mulungu wokoma mtima ndi wachifundo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero31 Komabe mwachifundo chanu chachikulu simuwatheretu kapena kuwataya pakuti ndinu Mulungu wokoma mtima ndi wachifundo. Onani mutuwo |