Nehemiya 9:30 - Buku Lopatulika30 Koma munawalekerera zaka zambiri, ndi kuwachitira umboni ndi mzimu wanu, mwa aneneri anu, koma sanamvere; chifukwa chake munawapereka m'dzanja la mitundu ya anthu a m'dziko. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201430 Koma munawalekerera zaka zambiri, ndi kuwachitira umboni ndi mzimu wanu, mwa aneneri anu, koma sanamvere; chifukwa chake munawapereka m'dzanja la mitundu ya anthu a m'dziko. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa30 Mudaŵapirira zaka zambiri ndipo munkaŵachenjeza ndi mzimu wanu kudzera mwa aneneri anu, komabe sadafune kutchera khutu. Nchifukwa chake mudaŵapereka kwa anthu a m'maiko ena. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero30 Munapirira nawo kwa zaka zambiri. Munkawachenjeza ndi Mzimu wanu kudzera mwa aneneri anu, koma iwo sankakumverani. Choncho munawapereka mʼmanja mwa anthu a mayiko ena. Onani mutuwo |