Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Nehemiya 9:3 - Buku Lopatulika

3 Naimirira poima pao, nawerenga m'buku la chilamulo cha Yehova Mulungu wao limodzi la magawo anai a tsiku; ndi limodzi la magawo anai anawulula, napembedza Yehova Mulungu wao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

3 Naimirira poima pao, nawerenga m'buku la chilamulo cha Yehova Mulungu wao limodzi la magawo anai a tsiku; ndi limodzi la magawo anai anawulula, napembedza Yehova Mulungu wao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

3 Anthuwo adaimirira pomwepo, ndipo adamva mau a m'buku la Malamulo a Chauta akuŵaŵerenga nthaŵi yokwanira maora atatu. Pa maora atatu enanso, anthuwo ankaulula machimo ao namapembedza Chauta, Mulungu wao.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

3 Anthuwo anayimirira pomwepo, ndipo anamva mawu a mʼbuku la malamulo a Yehova akuwerengedwa kwa maora enanso atatu ndipo anakhala maora ena atatu akuwulula machimo awo ndi kupembedza Yehova Mulungu wawo.

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 9:3
4 Mawu Ofanana  

Tsiku lomwelo anawerenga m'buku la Mose m'makutu a anthu, napeza m'menemo kuti Aamoni ndi Amowabu asalowe mu msonkhano wa Mulungu kunthawi yonse;


nabatizidwa ndi iye mu mtsinjewo wa Yordani, alikuwulula machimo ao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa