Nehemiya 9:21 - Buku Lopatulika21 Ndipo munawalera zaka makumi anai m'chipululu, osasowa kanthu iwo; zovala zao sizinathe, ndi mapazi ao sanatupe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201421 Ndipo munawalera zaka makumi anai m'chipululu, osasowa kanthu iwo; zovala zao sizinatha, ndi mapazi ao sanatupe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa21 Mudaŵasunga zaka makumi anai m'chipululu ndipo nthaŵi yonseyo sankasoŵa kanthu. Zovala zao sizidathe, mapazi aonso sadatupe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero21 Munawasunga zaka makumi anayi mʼchipululu ndipo sanasowe kanthu kalikonse. Zovala zawo sizinathe kapena mapazi awo kutupa.” Onani mutuwo |