Nehemiya 9:20 - Buku Lopatulika20 Munawapatsanso mzimu wanu wokoma kuwalangiza, ndipo simunawamane mana anu pakamwa pao; munawapatsanso madzi pa ludzu lao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Munawapatsanso mzimu wanu wokoma kuwalangiza, ndipo simunawamana mana anu pakamwa pao; munawapatsanso madzi pa ludzu lao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Inu mudaŵapatsa mzimu wanu wabwino kuti aziŵalangiza. Simudaŵamane chakudya cha mana chija, ndipo mudaŵapatsa madzi akumwa, kuti aphe ludzu lao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Inu munawapatsa mzimu wanu wabwino kuti uwalangize. Inu simunawamane chakudya cha mana chija, ndipo munawapatsa madzi akumwa. Onani mutuwo |