Nehemiya 7:72 - Buku Lopatulika72 Zopereka za anthu otsala ndizo madariki agolide zikwi makumi awiri, ndi miyeso ya siliva zikwi ziwiri, ndi malaya a ansembe makumi asanu ndi limodzi mphambu asanu ndi awiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201472 Zopereka za anthu otsala ndizo madariki agolide zikwi makumi awiri, ndi miyeso ya mina ya siliva zikwi ziwiri, ndi malaya a ansembe makumi asanu ndi limodzi mphambu asanu ndi awiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa72 Ndipo anthu onse otsala adapereka ndalama zagolide za makilogaramu 168, ndalama zasiliva zamakilogaramu 140, ndiponso mikanjo ya ansembe yokwanira 67. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero72 Anthu ena onse otsala anapereka ndalama zagolide zokwana makilogalamu 168, ndalama za siliva zokwana makilogalamu 140, ndiponso zovala za ansembe 67. Onani mutuwo |